LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsa. 2
  • July 2-8

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 2-8
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 July tsa. 2

July 2-8

LUKA 6-7

  • Nyimbo 109 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Tizipimila Ena Mowolowa Manja”: (10 min.)

    • Luka 6:37—Ngati timakhululukila anthu, nawonso adzatikhululukila (“Pitilizani kukhululukila anthu macimo awo ndipo macimo anunso adzakhululukidwa” nwtsty mfundo younikila; w08 5/15 peji 9 mapa. 13-14)

    • Luka 6:38—Tiyenela kukhala na cizoloŵezi cokhala wopatsa (“Khalani opatsa” nwtsty mfundo younikila)

    • Luka 6:38—Mlingo umene timapimila anthu ena, iwonso adzatipimila umenewo (“m’matumba anu” nwtsty mfundo younikila)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Luka 6:12, 13—Kodi Yesu anapeleka bwanji citsanzo cabwino kwa Akhristu pofuna kupanga zosankha zazikulu? (w07 8/1 peji 6 pala. 1)

    • Luka 7:35—Kodi mau a Yesu angatithandize bwanji ngati anthu ena atinenela misece? (“ana ake” nwtsty mfundo younikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Luka 7:36-50

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Kubwelelako Koyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) bhs mape. 197-198 mapa. 4-5

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 108

  • Tengelani Kuwolowa Manja kwa Yehova: (15 min.) Tambitsani vidiyoyi. Ndiyeno kambilanani mafunso aya:

    • Kodi Yehova na Yesu anaonetsa bwanji kuti ni owolowa manja?

    • Kodi Yehova amadalitsa bwanji kuwolowa manja kwathu?

    • Kodi kukhululuka mowolowa manja kumatanthauza ciani?

    • Kodi tingakhale owolowa manja na nthawi yathu m’njila ziti?

    • Tingaonetse bwanji kuwolowa manja poyamikila ena?

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 27

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 57 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani