LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 October tsa. 2
  • Pewani Kupembedza Mafano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pewani Kupembedza Mafano
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Tiyenela Kum’lambila Motani Mulungu Kuti Tim’kondweletse?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Khamu Lalikulu Losaŵelengeka Likudalitsidwa na Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Kulambila Koona Kudzawonjezela Cimwemwe Canu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 October tsa. 2
Aisiraeli akuvina mozungulila mwana wa ng’ombe wagolide.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 31-32

Pewani Kupembedza Mafano

32:1, 4-6, 9, 10

Cioneka kuti Aisiraeli anatengela maganizo a Aiguputo pa nkhani ya kulambila mafano. Masiku ano, munthu angalambile mafano m’njila zosiyana-siyana, ndipo zina zingakhale zovuta kuzizindikila. N’zoonekelatu kuti sitingayambe kulambila mafano eni-eni ooneka. Koma kungakhale kupembedza mafano ngati tilola zilakolako zathu zadyela kutilepheletsa kulambila Yehova na mtima wonse.

Zithunzi: Banja likucita zinthu zimene limacita masiku onse. 1. Tate akugwila nchito ya ukalipentala pa ovataimu. 2. Mwana akucita maseŵela a pakompyuta. 3. Mayi akugula zinthu zambili m’shopu.

Ni zinthu ziti pa umoyo wanga wa tsiku na tsiku zimene zinganiceutse pa kulambila Yehova? Nanga ningacite ciani kuti zinthuzo zisamanilamulile?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani