LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 34
  • N’dzayenda mu Umphumphu Wanga

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • N’dzayenda mu Umphumphu Wanga
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika
    Imbirani Yehova
  • Khalanibe na Mtima Wamphumphu!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Cimwemwe Cathu Camuyaya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 34

NYIMBO 34

N’dzayenda mu Umphumphu Wanga

Yopulinta

(Salimo 26)

  1. 1. Mlengi wanga, ine nikupempha

    Kuti mufufuze za mu mtima mwanga.

    Muniyese, O niweluzeni;

    Mudzapeza kuti nidalila imwe.

    (KOLASI)

    Koma ine, nikulonjezani

    Kuti nidzakhala wokhulupilika.

  2. 2. Sinikhala na anthu ocimwa,

    Nimapewa onse ocita zoipa.

    Conde m’saniononge pamodzi

    Ndi anthu ankhanza, ozonda co’nadi.

    (KOLASI)

    Koma ine, nikulonjezani

    Kuti nidzakhala wokhulupilika.

  3. 3. Nimakonda nyumba yanu M’lungu.

    Nimasangalala kulambila imwe.

    Nidzakulambilani mokondwa,

    Nidzaimba nyimbo zokutamandani.

    (KOLASI)

    Koma ine, nikulonjezani

    Kuti nidzakhala wokhulupilika.

(Onaninso Sal. 25:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani