LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 155
  • Cimwemwe Cathu Camuyaya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cimwemwe Cathu Camuyaya
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Cimwemwe Khalidwe Locokela kwa Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Tamandani Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi
    Imbirani Yehova
  • Khulupilila Coonadi Iwe Mwini
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 155

NYIMBO 155

Cimwemwe Cathu Camuyaya

Yopulinta

(Salimo 16:11)

  1. 1. Kumwamba kuli nyenyezi

    ndipo ziwala.

    Munakongoletsa usana

    na usiku.

    Manja anu anapanga

    zinthu zonse mukondwela

    Mukaziona.

    (KOLASI)

    Cilengedwe canu M’lungu

    Na uthenga wa Ufumu

    Zimatikondweletsa.

    Cikondi canu cosatha

    Ndiye cuma camuyaya.

    Ndimwe cimwemwe cathu.

    Inde, ca muyaya.

  2. 2. Yehova tili na zonse

    zosangalatsa—

    Zonse tiona na maso,

    zikhudza mtima.

    Mwatipatsa umuyaya

    Mumitima yathu,

    Na cimwemwe cosatha.

    (KOLASI)

    Cilengedwe canu M’lungu

    Na uthenga wa Ufumu

    Zimatikondweletsa.

    Cikondi canu cosatha

    Ndiye cuma camuyaya.

    Ndimwe cimwemwe cathu.

    Inde, ca muyaya.

    (BILIJI)

    Munapeleka Yesu

    Kuti atifele

    Sitikanapeza cimwemwe

    Popanda nsembe yake.

    (KOLASI)

    Cilengedwe canu M’lungu

    Na uthenga wa Ufumu,

    Zimatikondweletsa.

    Cikondi canu cosatha

    Ndiye cuma camuyaya.

    Ndimwe cimwemwe cathu

    Inde, ca muyaya.

    (KOLASI)

    Cilengedwe canu M’lungu

    Na uthenga wa Ufumu

    Zimatikondweletsa

    Cikondi canu cosatha

    Ndiye cuma camuyaya

    Ndimwe cimwemwe cathu

    Inde, ca muyaya.

(Onaninso Sal. 37:4; 1 Akor. 15:28.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani