LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 33
  • Tulila Yehova Nkhawa Zako

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tulila Yehova Nkhawa Zako
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
    Imbirani Yehova
  • Abusa ni Mphatso za Amuna
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Abusa Ndi Mphatso za Amuna
    Imbirani Yehova
  • “Umutulile Yehova Nkhawa Zako”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 33

NYIMBO 33

Tulila Yehova Nkhawa Zako

Yopulinta

(Salimo 55)

  1. 1. Conde nipempha Yehova

    Muniyankhe pemphelo.

    Mvelani kulila kwanga,

    Ndipo nithandizeni.

    (KOLASI)

    Uzani Yehova nkhawa,

    Iye adzakuthandizani.

    Adzakutsogolelani

    Kuti mutetezeke.

  2. 2. Sembe nenze monga nkhunda,

    Sembe nambululuka,

    Kuthaŵa adani anga

    Kuti asanipeze.

    (KOLASI)

    Uzani Yehova nkhawa,

    Iye adzakuthandizani.

    Adzakutsogolelani

    Kuti mutetezeke.

  3. 3. Yehova ‘katitonthoza

    Timapeza mtendele.

    Iye adzatithandiza

    Tisakhale na nkhawa.

    (KOLASI)

    Uzani Yehova nkhawa,

    Iye adzakuthandizani.

    Adzakutsogolelani

    Kuti mutetezeke.

(Onaninso Sal. 22:5; 31:1-24.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani