LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 107
  • Cikondi ca Umulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cikondi ca Umulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Cikondi Khalidwe Lamtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mmene Tingalimbikitsile Cikondi Cathu pa Ena
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 107

NYIMBO 107

Cikondi ca Umulungu

Yopulinta

(1 Yohane 4:19)

  1. 1. Timaphunzila cikondi kwa M’lungu,

    Poona citsanzo

    Wationetsa mu zocita zake,

    Kuti ise tim’tengele.

    Polola kuti Yesu atifele,

    Kuti ’se anthu tikhululukidwe.

    Cikondi cake ni copambanadi!

    Njila zake ni zacikondi.

  2. 2. Cikondi cathu poyenda na M’lungu,

    Cikula kwambili.

    Citithandiza kukonda abale,

    Nthawi zonse, inde onse.

    Okonda M’lungu na kuzonda m’bale

    Anama ndithu, izo n’zosatheka.

    Tisasungile abale zifukwa,

    Cikondici ni ca zoona.

  3. 3. Cikondi cathu cimatipangitsa

    Kukhala pamodzi.

    Ndipo Yehova amasangalala

    Tikakhala capamodzi.

    Cikondi cathu na cisangalalo

    Tizionetse pomutumikila.

    Mwa Mau ake na abale athu

    Timaona cikondi cake.

(Onaninso Aroma 12:10; Aef. 4:3; 2 Pet. 1:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani