- 
	                        
            
            Numeri 22:16, 17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        16 Iwo anapita kwa Balamu nʼkukamuuza kuti: “Balaki mwana wa Zipori wanena kuti, ‘Musalole kuti china chilichonse chikulepheretseni kubwera kwa ine, 17 chifukwa ndidzakupatsani mphoto yaikulu, ndipo ndidzachita chilichonse chimene mungandiuze. Chonde tabwerani mudzatemberere anthuwa.’” 
 
- 
                                        
- 
	                        
            
            Numeri 24:10, 11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        10 Kenako Balaki anapsera mtima Balamu. Ndiyeno Balaki anawomba mʼmanja mokwiya nʼkuuza Balamu kuti: “Ndinakuitana kuti udzatemberere adani anga,+ koma iwe wawadalitsa kwambiri maulendo atatu onsewa. 11 Nyamuka pompano uzipita kwanu. Ine ndimafuna ndikupatse mphoto,+ koma taona! Yehova wakulepheretsa kulandira mphoto.” 
 
-