Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 28:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Mudzadzala mbewu zambiri mʼmunda, koma mudzakolola zochepa+ chifukwa dzombe lidzadya mbewuzo.

  • Yoweli 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Zinthu zimene ziwala zowononga zinasiya zinadyedwa ndi dzombe lambirimbiri.+

      Zimene dzombelo linasiya zinadyedwa ndi ana a dzombe opanda mapiko.

      Ndipo zimene ana a dzombe opanda mapiko anasiya zinadyedwa ndi dzombe losakaza.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani