-
Numeri 15:18, 19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 “Lankhula ndi Aisiraeli ndipo uwauze kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukupititsani, 19 muzikapereka chopereka kwa Yehova pa chakudya chilichonse chamʼdzikolo,+ chimene muzikadya.
-