Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 49:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ponena za Edomu, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti:

      “Kodi nzeru zinatha ku Temani?+

      Kodi anthu ozindikira sakuperekanso malangizo anzeru?

      Kodi nzeru zawo zinawola?

  • Maliro 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iwe mwana wamkazi wa Ziyoni,* chilango chimene anakupatsa chifukwa cha zolakwa zako chatha.

      Sadzakutenganso kupita nawe ku ukapolo.+

      Koma Mulungu adzatembenukira kwa iwe, mwana wamkazi wa Edomu, kuti aone zolakwa zako.

      Machimo ako adzawaika poyera.+

  • Ezekieli 25:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Edomu wabwezera zoipa kwa nyumba ya Yuda ndipo wapalamula mlandu waukulu chifukwa chowabwezera.+

  • Obadiya 10-13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani