Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Samueli 22:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mulungu wanga ndi thanthwe langa,+ ine ndimathawira kwa iye,

      Iye ndi chishango changa,+ nyanga* yanga ya chipulumutso* ndi malo anga achitetezo.*+

      Komanso ndi malo anga othawirako,+ mpulumutsi wanga+ amene amandipulumutsa kwa anthu achiwawa.

  • Salimo 20:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake.+

      Amamuyankha kuchokera kumwamba kwake koyera,

      Pomupulumutsa modabwitsa ndi dzanja lake lamanja.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani