Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 21:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno Ahabu anafunsa Eliya kuti: “Wandipeza kodi mdani wanga?”+ Eliya anayankha kuti: “Inde ndakupezani. Mulungu wanena kuti, ‘Chifukwa watsimikiza mtima kuti uchite zoipa pamaso pa Yehova,+ 21 ndikubweretsera tsoka ndipo ndidzaseseratu nyumba yako ndi kupha mwamuna* aliyense wa mʼbanja la Ahabu,+ ngakhalenso ooneka onyozeka ndi ofooka mu Isiraeli.+

  • 1 Mafumu 22:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mfumu ya Isiraeli inayankha Yehosafati kuti: “Patsala munthu mmodzi amene tingathe kufunsira kwa Yehova+ kudzera mwa iye, koma ndimadana naye kwambiri,+ chifukwa salosera zabwino zokhudza ine, koma zoipa zokhazokha.+ Dzina lake ndi Mikaya mwana wa Imula.” Koma Yehosafati anati: “Mfumu siyenera kulankhula choncho.”

  • 2 Mbiri 25:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho Yehova anakwiyira kwambiri Amaziya ndipo anatumiza mneneri kukamʼfunsa kuti: “Nʼchifukwa chiyani mukutsatira milungu yomwe sinapulumutse anthu awo mʼmanja mwanu?”+ 16 Mneneriyo atanena zimenezi, mfumuyo inamufunsa kuti: “Kodi tinakuika kuti ukhale mlangizi wa mfumu?+ Usiyiretu kunena zimenezi.+ Ukufuna kuti akuphe?” Choncho mneneriyo anasiya, koma anati: “Ndikudziwa kuti Mulungu wakonza zoti akuwonongeni chifukwa cha zimene mwachitazi ndiponso chifukwa simunamvere malangizo anga.”+

  • Mateyu 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani