Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Oweruza 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Oweruza 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Zitatero Yehova anakwiyira kwambiri Aisiraeli, moti anawapereka mʼmanja mwa adani amene anawaukira nʼkutenga zinthu zawo.+ Iye anawagulitsa kwa adani awo owazungulira+ moti sanathe kulimbana nawo.+

  • 2 Mbiri 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kwa nthawi yaitali, Aisiraeli anakhala opanda Mulungu woona, opanda wansembe woti aziwaphunzitsa ndiponso opanda malamulo.+

  • 2 Mbiri 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mtundu unkamenyana ndi mtundu wina ndiponso mzinda ndi mzinda wina, chifukwa Mulungu anawasiya kuti asokonezeke ndi mavuto osiyanasiyana.+

  • Salimo 106:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Mobwerezabwereza ankawapereka mʼmanja mwa anthu a mitundu ina,+

      Kuti anthu amene ankadana nawo aziwalamulira.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani