-
Yeremiya 50:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 “Thawani mʼBabulo,
Tulukani mʼdziko la Akasidi,+
Ndipo mukhale ngati mbuzi kapena nkhosa zamphongo zimene zikutsogolera gulu lonse.
-