Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 48:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tulukani mʼBabulo!+

      Thawani mʼmanja mwa Akasidi.

      Lengezani zimenezi mofuula komanso mosangalala. Uzani anthu zimenezi.+

      Zineneni kuti anthu azidziwe mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+

      Munene kuti: “Yehova wawombola mtumiki wake Yakobo.+

  • Yeremiya 50:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 “Thawani mʼBabulo,

      Tulukani mʼdziko la Akasidi,+

      Ndipo mukhale ngati mbuzi kapena nkhosa zamphongo zimene zikutsogolera gulu lonse.

  • Yeremiya 51:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tulukani mʼBabulo nʼkuthawa,

      Ndipo pulumutsani moyo wanu.+

      Musawonongeke chifukwa cha zolakwa zake.

      Ino ndi nthawi yoti Yehova amubwezere.

      Mulungu akubwezera Babulo chifukwa cha zimene anachita.+

  • Zekariya 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Bwerani! Bwerani! Thawani mʼdziko lakumpoto,”+ watero Yehova.

      “Chifukwa ndinakubalalitsirani kumbali zonse za dziko lapansi,”+ watero Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani