Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 58:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ngati chifukwa cha Sabata mukupewa* kuchita zofuna zanu* pa tsiku langa lopatulika,+

      Ndipo mukanena kuti Sabata ndi tsiku losangalatsa kwambiri, tsiku lopatulika la Yehova, tsiku loyenera kulemekezedwa,+

      Ndipo mukalilemekeza mʼmalo mochita zofuna zanu ndiponso mʼmalo molankhula zopanda pake,

      14 Mukatero mudzasangalala kwambiri mwa Yehova,

      Ndipo ine ndidzakuchititsani kuti mukwere mʼmalo apamwamba a dziko lapansi.+

      Ndidzakuchititsani kuti mudye* zochokera mʼcholowa cha Yakobo kholo lanu,+

      Chifukwa pakamwa pa Yehova panena.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani