Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani inu okhala kumwamba, ndipo tcherani khutu inu okhala padziko lapansi,+

      Chifukwa Yehova wanena kuti:

      “Ndalera ana nʼkuwasamalira kuti akule,+

      Koma iwo andipandukira.+

  • Yesaya 31:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Aisiraeli inu, bwererani kwa Mulungu amene mwamupandukira mopanda manyazi.+

  • Yesaya 59:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ife tachimwa ndipo tamukana Yehova.

      Tabwerera mʼmbuyo nʼkumusiya Mulungu wathu.

      Tanena zinthu zopondereza ena komanso zopanduka.+

      Taganizira mabodza oti tinene ndipo talankhula mawu achinyengo mumtima mwathu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani