Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 17:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Salimanesere mfumu ya Asuri anabwera kudzamenyana naye+ ndipo Hoshiya anakhala mtumiki wake nʼkuyamba kupereka msonkho kwa iye.+

  • Yesaya 8:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako ndinagona ndi mneneri wamkazi* ndipo anakhala woyembekezera. Pambuyo pake anabereka mwana wamwamuna.+ Ndiyeno Yehova anandiuza kuti: “Umupatse dzina lakuti Maheri-salala-hasi-bazi, 4 chifukwa mwanayo asanadziwe kuitana kuti, ‘Ababa!’ kapena ‘Amama!’ chuma cha ku Damasiko ndi katundu wolandidwa ku Samariya zidzatengedwa nʼkupita nazo kwa mfumu ya Asuri.”+

  • Yesaya 10:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Choncho Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Anthu anga amene mukukhala mʼZiyoni, musachite mantha chifukwa cha Msuri amene ankakukwapulani ndi chikwapu+ ndiponso kukumenyani ndi ndodo, ngati mmene ankachitira Iguputo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani