Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Levitiko 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Numeri 35:33, 34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Musamadetse dziko limene mukukhalamo, chifukwa magazi ndi amene amadetsa dziko.+ Ndipo dziko limene ladetsedwa ndi magazi silingayeretsedwe ndi china chilichonse, kupatulapo magazi a munthu amene anakhetsa magaziyo.+ 34 Musamadetse dziko limene mukukhalamo, limene inenso ndikukhalamo, chifukwa ine Yehova ndikukhala pakati pa Aisiraeli.’”+

  • 2 Mbiri 33:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Manase anapitiriza kusocheretsa Yuda ndi anthu a ku Yerusalemu ndipo anawachititsa kuti azichita zinthu zoipa kuposa zimene ankachita anthu a mitundu yomwe Yehova anaiwononga pamaso pa Aisiraeli.+

  • Yeremiya 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Anthu amafunsa kuti: “Ngati mwamuna wathetsa ukwati ndi mkazi wake, ndipo mkaziyo akachokadi nʼkukakwatiwa ndi mwamuna wina, kodi mwamunayo angabwererenso kwa mkaziyo?”

      Kodi dzikoli silaipitsidwa kale kwambiri?+

      Yehova wanena kuti: “Iwe wachita uhule ndi amuna ambirimbiri.+

      Ndiye kodi pano ukufuna ubwererenso kwa ine?

  • Yeremiya 23:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzikoli ladzaza ndi anthu achigololo.+

      Chifukwa cha matemberero, dziko likulira maliro+

      Ndipo malo amʼchipululu odyetserako ziweto auma.+

      Zochita za anthuwa ndi zoipa ndipo akugwiritsa ntchito mphamvu zawo molakwika.

      11 “Aneneri ndi ansembe, onse aipitsidwa.*+

      Ndipo ngakhale mʼnyumba mwanga ndapezamo zoipa zimene akuchita,”+ akutero Yehova.

  • Maliro 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zimenezi zinachitika chifukwa cha machimo a aneneri ake ndi zolakwa za ansembe ake,+

      Amene anakhetsa magazi a anthu olungama mumzindawo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani