Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 32:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno Yehova anatumiza mngelo yemwe anapha msilikali aliyense wamphamvu,+ mtsogoleri ndiponso mkulu wa asilikali aliyense mumsasa wa mfumu ya Asuri, moti mfumuyo inabwerera kwawo mwamanyazi. Kenako inalowa mʼkachisi wa mulungu wake ndipo ena mwa ana ake anaipha ndi lupanga mʼkachisimo.+

  • Yesaya 37:37, 38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Choncho Senakeribu mfumu ya Asuri anachoka nʼkubwerera kukakhala ku Nineve.+ 38 Pamene Senakeribu ankaweramira mulungu wake Nisiroki mʼkachisi, ana ake Adarameleki ndi Sarezere anamupha ndi lupanga+ nʼkuthawira kudziko la Ararati.+ Kenako mwana wake Esari-hadoni+ anakhala mfumu mʼmalo mwake.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani