-
Yeremiya 25:27, 28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 “Ndiyeno ukawauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli wanena kuti: “Imwani ndipo muledzere, musanze ndi kugwa osadzukanso+ chifukwa cha lupanga limene ndikutumiza pakati panu.”’ 28 Ngati angakakane kulandira kapuyi mʼmanja mwako kuti amwe, ukawauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Mukuyenera kumwa basi.
-
-
Obadiya 16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Mmene wamwera vinyo paphiri langa loyera,
Ndi mmenenso mitundu ina yonse ya anthu izidzamwera mkwiyo wanga nthawi zonse.+
Iwo adzamwa ndi kugugudiza mkwiyo wanga,
Ndipo zidzakhala ngati sanakhalepo nʼkomwe.
-