Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 48:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Yehova wanena kuti:

      ‘Taonani! Mofanana ndi chiwombankhanga chimene chimatsika nʼkugwira chakudya chake,+

      Mdani adzatambasula mapiko ake nʼkugwira Mowabu.+

  • Yeremiya 49:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Chifukwa ine ndalumbira pa dzina langa kuti Bozira adzakhala chinthu chochititsa mantha,+ adzanyozedwa, adzawonongedwa ndi kutembereredwa ndipo mizinda yake yonse idzakhala mabwinja mpaka kalekale,” akutero Yehova.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani