Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yoswa 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Akanani ndi anthu onse a mʼdzikoli adzamva zimenezi, ndipo adzabwera nʼkufafaniza dzina lathu padziko lapansi. Ndiye mudzateteza bwanji dzina lanu lalikulu?”+

  • Salimo 25:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa cha dzina lanu, inu Yehova,+

      Mundikhululukire tchimo langa, ngakhale kuti ndi lalikulu.

  • Salimo 115:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 115 Ife sitikuyenera, inu Yehova, ife sitikuyenera,

      Koma ulemerero ukuyenera kupita ku dzina lanu+

      Chifukwa cha kukhulupirika kwanu komanso chikondi chanu chokhulupirika.+

       2 Musalole kuti anthu a mitundu ina azinena kuti:

      “Mulungu wawo ali kuti?”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani