Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Miyambo 28:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Munthu wokhulupirika adzalandira madalitso ambiri,+

      Koma amene akufuna kulemera mofulumira, sadzapitiriza kukhala wosalakwa.+

  • Yesaya 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Akalonga ako ndi osamva ndipo amagwirizana ndi anthu akuba.+

      Aliyense wa iwo amakonda ziphuphu ndipo amalakalaka kupatsidwa mphatso.+

      Mwana wamasiye samuweruza mwachilungamo,

      Ndipo ngakhale mlandu wa mkazi wamasiye safuna kuuweruza.+

  • Yakobo 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani