Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 13:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Uwu ndi uthenga wokhudza Babulo,+ umene Yesaya+ mwana wa Amozi anaona mʼmasomphenya:

  • Yesaya 13:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Babulo, amene ndi waulemerero kwambiri* kuposa maufumu onse,+

      Chinthu chokongola chimene Akasidi amachinyadira,+

      Adzakhala ngati Sodomu ndi Gomora pa nthawi imene Mulungu anawononga mizindayi.+

  • Yesaya 14:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 mudzanena mwambi uwu wonyoza mfumu ya Babulo:

      “Amene ankagwiritsa ntchito anzake mokakamiza uja wawonongedwa!

      Kuponderezedwa kuja kwatha ndithu!+

  • Yesaya 14:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani