Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 28:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndiyeno mʼchaka chomwecho, chaka cha 4, mʼmwezi wa 5, kumayambiriro kwa ulamuliro wa Zedekiya+ mfumu ya Yuda, mneneri Hananiya mwana wa Azuri, wa ku Gibiyoni,+ anauza Yeremiya mʼnyumba ya Yehova pamaso pa ansembe ndi anthu onse kuti: 2 “Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti, ‘Ndithyola goli la mfumu ya Babulo.+

  • Yeremiya 28:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Hananiya anauza anthu onse amene anali pamenepo kuti: “Yehova wanena kuti, ‘Mofanana ndi mmene ndathyolera goli ili, zaka ziwiri zisanathe,+ ndidzathyola goli la Nebukadinezara mfumu ya Babulo limene waveka mitundu yonse ya anthu.’” Zitatero, mneneri Yeremiya anachokapo.

  • Yeremiya 37:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tsopano ali kuti aneneri anu amene ankalosera kwa inu kuti, ‘Mfumu ya Babulo sidzabwera kudzamenyana ndi inu ndiponso dzikoliʼ?+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani