Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Danieli 5:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Dariyo+ Mmedi anapatsidwa ufumuwo ndipo anali ndi zaka pafupifupi 62.

  • Danieli 6:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno Dariyo anaona kuti ndi bwino kuti aike masatarapi* 120 oti aziyangʼanira zigawo zonse za ufumu wake.+ 2 Anaikanso nduna zapamwamba zitatu kuti ziziyangʼanira masatarapiwo ndipo Danieli anali mmodzi wa ndunazo.+ Masatarapiwo+ ankayenera kuuza nduna zimenezi chilichonse chimene chikuchitika nʼcholinga chakuti zinthu za mfumu zisawonongeke.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani