Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 118:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mwala umene omanga nyumba anaukana

      Wakhala mwala wapakona* wofunika kwambiri.+

  • Yesaya 50:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Msana wanga ndinaupereka kwa anthu amene ankandimenya

      Ndipo masaya anga ndinawapereka kwa anthu amene ankandizula ndevu.

      Sindinabise nkhope yanga kuti asaichitire zinthu zochititsa manyazi komanso kuti asailavulire.+

  • Yesaya 53:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye anaponderezedwa ndipo anatengedwa popanda kuweruzidwa mwachilungamo.

      Ndi ndani amene anaganizira tsatanetsatane wa mʼbadwo wa makolo ake?*

      Popeza iye anadulidwa mʼdziko la anthu amoyo.+

      Iye anakwapulidwa* chifukwa cha zolakwa za anthu anga.+

  • Danieli 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Luka 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani