Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb17.10 6
  • October 23-29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 23-29
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17.10 6

October 23-29

HOSEYA 8-14

  • Nyimbo Na. 153 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muzipereka Zinthu Zabwino Kwambiri kwa Yehova”: (10 min.)

    • Hos. 14:2​—Yehova amayamikira kwambiri nsembe zimene timamupatsa zomwe ndi “mawu apakamwa pathu” (w07 4/1 20 ¶2)

    • Hos. 14:4​—Yehova amakonda anthu amene amachita zonse zomwe angathe pomutumikira, amawakhululukira machimo, komanso amawaona ngati anzake (w11 2/15 16 ¶15)

    • Hos. 14:9​—Tikamayenda m’njira za Yehova timapindula kwambiri (jd 87 ¶11)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Hos. 10:12​—Kodi tiyenera kuchita chiyani kuti ‘tikolole zipatso za kukoma mtima kosatha’ kwa Yehova? (w05 11/15 28 ¶7)

    • Hos. 11:1​—Kodi mawu a mu vesili anakwaniritsidwa bwanji pa Yesu? (w11 8/15 10 ¶10)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Hos. 8:1-14

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) T-35

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) T-35​—Pitirizani kukambirana zokhudza kapepala kamene munamupatsa pa ulendo woyamba. Sonyezani mmene tingayankhire ngati mwininyumba akutsutsa mfundo inayake.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 152 ¶13-14—Sonyezani mmene tingafikire pamtima wophunzira wathu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 97

  • “Muzitumikira Yehova Nthawi Zonse”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Muzigwiritsa Ntchito Luso Lanu Kutumikira Yehova.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 9 ¶1-9, komanso tsamba 89

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 63 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani