Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno Mfumu Ahazi inalamula wansembe Uliya+ kuti: “Paguwa lansembe lalikululi uziwotchapo nsembe yopsereza yam’mawa,+ nsembe yambewu yamadzulo,+ nsembe yopsereza ya mfumu+ ndi nsembe yake yambewu, nsembe yopsereza ya anthu onse a m’dzikoli ndi nsembe yawo yambewu, ndiponso nsembe zawo zachakumwa. Magazi onse a nsembe yopsereza ndi magazi onse a nsembe zina uziwawaza paguwa langali. Koma guwa lansembe lamkuwalo, ndiona chochita nalo.”

  • Machitidwe 26:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndipo mafuko athu 12 akuyembekezera kuona kukwaniritsidwa kwa lonjezo limeneli, mwa kumuchitira utumiki wopatulika mosalekeza usana ndi usiku.+ Chotero Mfumu, Ayuda akundiimba mlandu chifukwa cha chiyembekezo chimenechi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena