-
1 Mbiri 21:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Zaka zitatu za njala+ kapena miyezi itatu yoti adani anu akuseseni+ ndi kukuphani ndi lupanga lawo, kapenanso masiku atatu a lupanga la Yehova,+ lomwe ndi mliri+ umene udzagwe m’dziko lanu mpaka mngelo wa Yehova atasakaza+ madera onse a Isiraeli.’ Ndiye tandiuzani zoti ndikayankhe kwa Amene wanditumayo.”
-