Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno Yehova anauza Mose kuti: “Taona, ndakuika kuti ukhale Mulungu kwa Farao,+ ndipo Aroni m’bale wako akhala mneneri wako.+

  • Ekisodo 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chotero Mose ndi Aroni anapita kwa Farao ndi kuchita ndendende mmene Yehova anawalamulira. Pamenepo Aroni anaponya ndodo yake patsogolo pa Farao ndi atumiki ake, ndipo ndodoyo inasanduka njoka yaikulu.

  • Salimo 119:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  46 Komanso ndidzanena za zikumbutso zanu pamaso pa mafumu,+

      Ndipo sindidzachita manyazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena