Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Patapita kanthawi, panafika mwana wamkazi wa Farao kudzasamba mumtsinje wa Nailo. Ndipo atsikana omutumikira anali kuyenda m’mphepete mwa mtsinjewo. Kenako iye anaona kabokosi kaja kali pakati pa mabango. Nthawi yomweyo anatuma kapolo wake wamkazi kuti akakatenge.+

  • Ekisodo 8:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Yehova anauza Mose kuti: “Mawa ulawirire m’mawa kwambiri kukakumana ndi Farao.+ Iyetu adzapita kumtsinje, ndipo ukamuuze kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Lola anthu anga apite kuti akanditumikire.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena