Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndipo ndikukuuza kuti: Lola mwana wanga apite kuti akanditumikire. Koma ngati ukukana kumulola kuti apite, taona ndidzapha mwana wako wamwamuna, mwana wako woyamba kubadwa.”’”+

  • Ekisodo 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ngati upitiriza kukana kuti apite, ndigwetsera dziko lako lonse mliri wa achule.+

  • Salimo 68:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndithudi, Mulungu adzaphwanya mitu ya adani ake kukhala zibenthuzibenthu,+

      Adzaphwanya liwombo latsitsi la aliyense woyenda m’njira yochimwa.+

  • Miyambo 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 N’chifukwa chake tsoka lake lidzabwere mwadzidzidzi.+ Adzathyoledwa modzidzimutsa, ndipo sadzachira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena