Ekisodo 10:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Dzombelo lidzakuta nthaka yonse ndipo simudzatha kuona dothi. Lidzadya chilichonse chotsalira. Ndithu, lidzadya chilichonse chimene matalala anakusiyirani. Ndipo lidzadya mitengo yanu yonse imene yaphuka.+ Yobu 38:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Kodi unalowapo munkhokwe ya chipale chofewa,+Kapena umaziona nkhokwe za matalala,+ Salimo 78:47 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 47 Anapha mitengo yawo ya mpesa ndi mvula yamatalala.+Anapha mitengo yawo ya mkuyu ndi matalala.+ Salimo 105:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Anawagwetsera matalala m’malo mwa mvula,+Anawagwetseranso moto woyaka, walawilawi m’dziko lawo.+
5 Dzombelo lidzakuta nthaka yonse ndipo simudzatha kuona dothi. Lidzadya chilichonse chotsalira. Ndithu, lidzadya chilichonse chimene matalala anakusiyirani. Ndipo lidzadya mitengo yanu yonse imene yaphuka.+
22 Kodi unalowapo munkhokwe ya chipale chofewa,+Kapena umaziona nkhokwe za matalala,+ Salimo 78:47 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 47 Anapha mitengo yawo ya mpesa ndi mvula yamatalala.+Anapha mitengo yawo ya mkuyu ndi matalala.+ Salimo 105:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Anawagwetsera matalala m’malo mwa mvula,+Anawagwetseranso moto woyaka, walawilawi m’dziko lawo.+