Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ine ndidzakhala ndi iwe kulikonse kumene udzapite,+ ndipo ndidzawononga ndi kuchotsa adani ako onse pamaso pako.+ Ndidzakupangira dzina lotchuka,+ lofanana ndi dzina la anthu otchuka amene ali m’dziko.

  • Esitere 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Izi zinali choncho chifukwa Moredekai anali ndi udindo waukulu+ m’nyumba ya mfumu ndipo anatchuka+ m’zigawo zonse chifukwa mphamvu zake zinali kukulirakulira.+

  • Machitidwe 7:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Chotero Mose anaphunzira nzeru+ zonse za Aiguputo. Ndipo anali wamphamvu m’mawu+ ndi m’zochita zake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena