Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 33:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma iyeyo anapita patsogolo pawo, n’kuyamba kugwada, n’kumaweramitsa nkhope yake pansi mpaka nthawi 7. Anachita zimenezi mpaka kufika pafupi ndi m’bale wakeyo.+

  • 2 Samueli 14:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Chotero Yowabu anapita kukaonana ndi mfumu ndipo anaiuza mawu amenewa. Ndiyeno mfumu inaitanitsa Abisalomu, moti iye anabwera kudzaonana ndi mfumu. Abisalomu atafika anagwada ndi kuwerama, kenako anadzigwetsa pansi pamaso pa mfumu. Zitatero, mfumu inapsompsona Abisalomu.+

  • Aroma 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pokonda abale,+ khalani ndi chikondi chenicheni pakati panu. Posonyezana ulemu,+ khalani patsogolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena