Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Tsopano Kora+ mwana wa Izara,+ mwana wa Kohati,+ mwana wa Levi,+ anagwirizana ndi adzukulu a Rubeni,+ omwe ndi Datani+ ndi Abiramu+ ana a Eliyabu,+ komanso Oni mwana wa Pelete, kuti aukire.

  • Numeri 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pambuyo pake, Mose anatuma mthenga kukaitana Datani ndi Abiramu,+ ana a Eliyabu. Koma iwo anayankha kuti: “Ife sitibwerako kumeneko!+

  • Numeri 16:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Nthawi yomweyo anthuwo anachoka kumbali zonse za mahema a Kora, Datani ndi Abiramu. Zitatero, Datani ndi Abiramu anatuluka n’kuima pamakomo a mahema awo,+ limodzi ndi akazi awo, ana awo.

  • Salimo 106:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo dziko lapansi linatseguka ndipo linameza Datani,+

      Ndi kufotsera msonkhano wa Abiramu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena