Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 34:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Musankhe mtsogoleri mmodzi pa fuko lililonse, kuti akathandize kugawa cholowa cha malo.+

  • Deuteronomo 32:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Pamene Wam’mwambamwamba anapereka cholowa kwa mitundu,+

      Pamene analekanitsa ana a Adamu,+

      Anaika malire a anthu+

      Poganizira chiwerengero cha ana a Isiraeli.+

  • Yoswa 19:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Zimenezi ndiye zigawo za cholowa chimene wansembe Eleazara, Yoswa mwana wa Nuni, ndi atsogoleri a mafuko a ana a Isiraeli, anagawira anthu.+ Anagawa dzikolo pochita maere ku Silo+ pamaso pa Yehova, pakhomo la chihema chokumanako,+ ndipo anamaliza kuligawa dzikolo.

  • Machitidwe 17:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndipo kuchokera mwa munthu mmodzi+ anapanga mtundu wonse wa anthu,+ kuti akhale padziko lonse lapansi.+ Iye anakhazikitsa nthawi zoikidwiratu+ komanso anaika malire achikhalire a malo oti anthu azikhala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena