Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 32:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:26; 30:19

Deuteronomo 32:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yob 29:22; Yes 55:10
  • +Miy 19:12; Ho 14:5
  • +Sl 72:6
  • +Mik 5:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2020, tsa. 10

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    4/2016, ptsa. 3-4

Deuteronomo 32:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:5; Sl 105:1; Yoh 17:26
  • +1Mb 29:11; Sl 145:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2020, ptsa. 10-11

Deuteronomo 32:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 22:31; Sl 18:2; 19:7; Yak 1:17
  • +Sl 33:5; 67:4; Da 4:37
  • +De 7:9; Ne 9:33; Sl 98:3; Ahe 10:23; 1Pe 4:19
  • +De 25:16; Yob 34:10; Aro 3:5
  • +Ge 18:25; Sl 92:15; 99:4; Ho 14:9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Yandikirani, tsa. 112

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/2009, tsa. 14

    9/15/2004, tsa. 27

    3/1/1989, ptsa. 19-22

Deuteronomo 32:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:27; Owe 2:19; Sl 14:1
  • +Yes 1:4; Yer 15:6; Yak 1:14
  • +Sl 78:8; Lu 9:41; Afi 2:15

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/1988, tsa. 10

Deuteronomo 32:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 1:2
  • +Yer 4:22
  • +Eks 4:22; De 32:18; 2Sa 7:23; Yes 63:16
  • +Sl 55:22

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2008, tsa. 5

Deuteronomo 32:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 63:11
  • +Eks 13:14; Sl 44:1
  • +Sl 78:3

Deuteronomo 32:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 10:5; Sl 115:16
  • +Ge 11:9
  • +De 2:5, 19; Mac 17:26
  • +Ge 15:18; Eks 23:31; Sl 105:44

Deuteronomo 32:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:16; 19:5; De 7:6; 26:19
  • +1Sa 10:1; Sl 74:2; 78:71

Deuteronomo 32:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 8:15; Ho 13:5
  • +Sl 107:4; Yer 2:6
  • +Ne 9:19
  • +Ne 9:20; Sl 8:4
  • +Sl 17:8; Zek 2:8

Deuteronomo 32:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 31:5
  • +Eks 19:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/2001, tsa. 9

    6/15/2001, tsa. 26

    6/15/1996, tsa. 11

Deuteronomo 32:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:31
  • +Yes 43:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/2001, tsa. 9

    6/15/2001, tsa. 26

Deuteronomo 32:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 33:29; Yes 58:14
  • +De 8:8
  • +Sl 81:16
  • +Yob 29:6

Deuteronomo 32:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 18:8
  • +Eze 39:18
  • +Sl 147:14
  • +Ge 49:11

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2015, tsa. 15

    9/15/2004, tsa. 27

    5/1/1989, tsa. 16

Deuteronomo 32:15

Mawu a M'munsi

  • *

    Kutanthauza “Wolungama.” Limeneli ndi dzina laulemu la Isiraeli.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 33:5; Yes 44:2
  • +Ho 4:16
  • +De 31:20; Ne 9:25; Sl 73:7
  • +Yes 1:4; 51:13; Ho 13:6
  • +2Sa 22:47; Sl 89:26; 95:1

Deuteronomo 32:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 14:22; 1Ak 10:22
  • +Owe 2:12
  • +2Mf 23:13; Eze 8:17

Deuteronomo 32:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 17:7; Sl 106:37; 1Ak 10:20
  • +De 28:64
  • +Owe 5:8

Deuteronomo 32:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 106:21; Yes 17:10; Yer 2:32; 3:21
  • +De 4:34

Deuteronomo 32:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 2:14; Sl 78:59; 106:40

Deuteronomo 32:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:17; Yob 34:29; Sl 30:7
  • +De 32:5; Yes 65:2; Mt 17:17
  • +Yes 1:2; 30:9

Deuteronomo 32:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 96:5; Yes 44:10; 1Ak 8:4; 10:20
  • +1Sa 12:10, 21; 1Mf 16:13; Mac 14:15
  • +Ho 1:10; 2:23; Aro 9:25; 11:11; 1Pe 2:10
  • +Aro 10:19

Deuteronomo 32:22

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Zakumapeto 5.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 21:9; Yer 15:14; Mlr 4:11
  • +Amo 9:2
  • +Zef 3:8
  • +Hab 3:10

Deuteronomo 32:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:24; De 28:15
  • +Sl 7:13; Eze 5:16

Deuteronomo 32:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:53
  • +De 28:22
  • +De 28:21; Amo 4:10
  • +Le 26:22; Yer 15:3; Eze 5:17
  • +Nu 21:6; Yer 8:17; Amo 9:3

Deuteronomo 32:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 9:16; Mlr 1:20
  • +Yer 9:21; Eze 7:15
  • +2Mb 36:17
  • +Mlr 2:21

Deuteronomo 32:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:33; De 28:25; Eze 20:23; Lu 21:24
  • +De 9:14

Deuteronomo 32:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 12:22; Eze 20:14
  • +Eks 32:12; Nu 14:16
  • +Sl 115:2; 140:8
  • +Yes 37:24

Deuteronomo 32:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 106:13; 107:11; Lu 7:30
  • +Yes 6:10; 27:11; Mt 13:15

Deuteronomo 32:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 81:13; Miy 1:5; 27:11
  • +Sl 107:43; Ho 14:9; 1Ti 4:15
  • +Yer 2:19; Mlr 1:9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 35

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2008, ptsa. 8-11

    7/1/1999, tsa. 32

Deuteronomo 32:30

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 24:24; Yes 30:17
  • +Owe 2:14; 1Sa 12:9; Sl 44:12; Yes 50:1

Deuteronomo 32:31

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 14:25; 1Sa 2:2
  • +1Sa 4:8; Eza 1:3; Da 2:47

Deuteronomo 32:32

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 1:10; Yuda 7
  • +Yes 5:4; Yer 2:21

Deuteronomo 32:33

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 58:4; 140:3

Deuteronomo 32:34

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ho 13:12; Aro 2:5

Deuteronomo 32:35

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 94:1; Nah 1:2; Aro 12:19; Ahe 10:30
  • +Sl 9:15; 73:18; Yes 8:15
  • +Yer 10:15; Lu 19:44
  • +Yes 30:13; Hab 2:3; 2Pe 2:3

Deuteronomo 32:36

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 7:8; 96:13; Ahe 10:30
  • +Owe 2:18; Sl 90:13; 106:45; 135:14

Deuteronomo 32:37

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 10:14; Yer 2:28
  • +De 32:31

Deuteronomo 32:38

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eze 16:19; 1Ak 10:20
  • +Ho 2:8; 1Ak 10:21
  • +Owe 10:14
  • +Amo 9:2

Deuteronomo 32:39

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 41:4; 48:12
  • +De 4:35; Yes 45:5
  • +1Sa 2:6; 2Mf 5:7; Sl 68:20
  • +Nu 12:13; 2Mb 21:18
  • +Yer 17:14; Ho 6:1
  • +Yes 43:13

Deuteronomo 32:40

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 6:8; Yes 45:23; Ahe 6:13
  • +Sl 90:2; 1Ti 1:17; Chv 10:6

Deuteronomo 32:41

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 7:12; Eze 21:10
  • +Yes 66:16; Nah 1:3
  • +De 32:35; Yes 1:24; 59:18; 66:6; Nah 1:2
  • +Eks 20:5

Deuteronomo 32:42

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 32:23
  • +Yes 34:6; Eze 38:21
  • +Yos 10:17, 26; 1Sa 15:33

Deuteronomo 32:43

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 12:3; 1Mf 8:43; Aro 3:29; 15:10
  • +2Mf 9:7; Chv 6:10
  • +De 32:41; Mik 5:15; Lu 21:22

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1998, ptsa. 12, 17

    4/15/1991, ptsa. 12-13

Deuteronomo 32:44

Mawu a M'munsi

  • *

    Dzina lakale la Yoswa.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:22; Chv 15:3
  • +Nu 11:28; De 31:23

Deuteronomo 32:46

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:6; 11:18
  • +De 6:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/15/2001, tsa. 19

    8/15/1988, ptsa. 10-12

Deuteronomo 32:47

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ti 3:16; Ahe 4:12
  • +Le 18:5; De 30:19; Aro 10:5
  • +Miy 3:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    2/2023, tsa. 3

    Nsanja ya Olonda,

    4/15/2008, ptsa. 5-6

Deuteronomo 32:49

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 27:12
  • +De 34:1
  • +Ge 10:19; 15:18; Yos 1:3

Deuteronomo 32:50

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 34:5
  • +Nu 20:28; 33:38

Deuteronomo 32:51

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:12; 27:14
  • +Nu 20:13
  • +Le 10:3; 22:32; Yes 8:13; Mt 6:9

Deuteronomo 32:52

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 27:13; De 3:27; 34:4

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 32:1De 4:26; 30:19
Deut. 32:2Yob 29:22; Yes 55:10
Deut. 32:2Miy 19:12; Ho 14:5
Deut. 32:2Sl 72:6
Deut. 32:2Mik 5:7
Deut. 32:3Eks 34:5; Sl 105:1; Yoh 17:26
Deut. 32:31Mb 29:11; Sl 145:3
Deut. 32:42Sa 22:31; Sl 18:2; 19:7; Yak 1:17
Deut. 32:4Sl 33:5; 67:4; Da 4:37
Deut. 32:4De 7:9; Ne 9:33; Sl 98:3; Ahe 10:23; 1Pe 4:19
Deut. 32:4De 25:16; Yob 34:10; Aro 3:5
Deut. 32:4Ge 18:25; Sl 92:15; 99:4; Ho 14:9
Deut. 32:5De 31:27; Owe 2:19; Sl 14:1
Deut. 32:5Yes 1:4; Yer 15:6; Yak 1:14
Deut. 32:5Sl 78:8; Lu 9:41; Afi 2:15
Deut. 32:6Yes 1:2
Deut. 32:6Yer 4:22
Deut. 32:6Eks 4:22; De 32:18; 2Sa 7:23; Yes 63:16
Deut. 32:6Sl 55:22
Deut. 32:7Yes 63:11
Deut. 32:7Eks 13:14; Sl 44:1
Deut. 32:7Sl 78:3
Deut. 32:8Ge 10:5; Sl 115:16
Deut. 32:8Ge 11:9
Deut. 32:8De 2:5, 19; Mac 17:26
Deut. 32:8Ge 15:18; Eks 23:31; Sl 105:44
Deut. 32:9Eks 15:16; 19:5; De 7:6; 26:19
Deut. 32:91Sa 10:1; Sl 74:2; 78:71
Deut. 32:10De 8:15; Ho 13:5
Deut. 32:10Sl 107:4; Yer 2:6
Deut. 32:10Ne 9:19
Deut. 32:10Ne 9:20; Sl 8:4
Deut. 32:10Sl 17:8; Zek 2:8
Deut. 32:11Yes 31:5
Deut. 32:11Eks 19:4
Deut. 32:12De 1:31
Deut. 32:12Yes 43:12
Deut. 32:13De 33:29; Yes 58:14
Deut. 32:13De 8:8
Deut. 32:13Sl 81:16
Deut. 32:13Yob 29:6
Deut. 32:14Ge 18:8
Deut. 32:14Eze 39:18
Deut. 32:14Sl 147:14
Deut. 32:14Ge 49:11
Deut. 32:15De 33:5; Yes 44:2
Deut. 32:15Ho 4:16
Deut. 32:15De 31:20; Ne 9:25; Sl 73:7
Deut. 32:15Yes 1:4; 51:13; Ho 13:6
Deut. 32:152Sa 22:47; Sl 89:26; 95:1
Deut. 32:161Mf 14:22; 1Ak 10:22
Deut. 32:16Owe 2:12
Deut. 32:162Mf 23:13; Eze 8:17
Deut. 32:17Le 17:7; Sl 106:37; 1Ak 10:20
Deut. 32:17De 28:64
Deut. 32:17Owe 5:8
Deut. 32:18Sl 106:21; Yes 17:10; Yer 2:32; 3:21
Deut. 32:18De 4:34
Deut. 32:19Owe 2:14; Sl 78:59; 106:40
Deut. 32:20De 31:17; Yob 34:29; Sl 30:7
Deut. 32:20De 32:5; Yes 65:2; Mt 17:17
Deut. 32:20Yes 1:2; 30:9
Deut. 32:21Sl 96:5; Yes 44:10; 1Ak 8:4; 10:20
Deut. 32:211Sa 12:10, 21; 1Mf 16:13; Mac 14:15
Deut. 32:21Ho 1:10; 2:23; Aro 9:25; 11:11; 1Pe 2:10
Deut. 32:21Aro 10:19
Deut. 32:22Sl 21:9; Yer 15:14; Mlr 4:11
Deut. 32:22Amo 9:2
Deut. 32:22Zef 3:8
Deut. 32:22Hab 3:10
Deut. 32:23Le 26:24; De 28:15
Deut. 32:23Sl 7:13; Eze 5:16
Deut. 32:24De 28:53
Deut. 32:24De 28:22
Deut. 32:24De 28:21; Amo 4:10
Deut. 32:24Le 26:22; Yer 15:3; Eze 5:17
Deut. 32:24Nu 21:6; Yer 8:17; Amo 9:3
Deut. 32:25Yer 9:16; Mlr 1:20
Deut. 32:25Yer 9:21; Eze 7:15
Deut. 32:252Mb 36:17
Deut. 32:25Mlr 2:21
Deut. 32:26Le 26:33; De 28:25; Eze 20:23; Lu 21:24
Deut. 32:26De 9:14
Deut. 32:271Sa 12:22; Eze 20:14
Deut. 32:27Eks 32:12; Nu 14:16
Deut. 32:27Sl 115:2; 140:8
Deut. 32:27Yes 37:24
Deut. 32:28Sl 106:13; 107:11; Lu 7:30
Deut. 32:28Yes 6:10; 27:11; Mt 13:15
Deut. 32:29Sl 81:13; Miy 1:5; 27:11
Deut. 32:29Sl 107:43; Ho 14:9; 1Ti 4:15
Deut. 32:29Yer 2:19; Mlr 1:9
Deut. 32:302Mb 24:24; Yes 30:17
Deut. 32:30Owe 2:14; 1Sa 12:9; Sl 44:12; Yes 50:1
Deut. 32:31Eks 14:25; 1Sa 2:2
Deut. 32:311Sa 4:8; Eza 1:3; Da 2:47
Deut. 32:32Yes 1:10; Yuda 7
Deut. 32:32Yes 5:4; Yer 2:21
Deut. 32:33Sl 58:4; 140:3
Deut. 32:34Ho 13:12; Aro 2:5
Deut. 32:35Sl 94:1; Nah 1:2; Aro 12:19; Ahe 10:30
Deut. 32:35Sl 9:15; 73:18; Yes 8:15
Deut. 32:35Yer 10:15; Lu 19:44
Deut. 32:35Yes 30:13; Hab 2:3; 2Pe 2:3
Deut. 32:36Sl 7:8; 96:13; Ahe 10:30
Deut. 32:36Owe 2:18; Sl 90:13; 106:45; 135:14
Deut. 32:37Owe 10:14; Yer 2:28
Deut. 32:37De 32:31
Deut. 32:38Eze 16:19; 1Ak 10:20
Deut. 32:38Ho 2:8; 1Ak 10:21
Deut. 32:38Owe 10:14
Deut. 32:38Amo 9:2
Deut. 32:39Yes 41:4; 48:12
Deut. 32:39De 4:35; Yes 45:5
Deut. 32:391Sa 2:6; 2Mf 5:7; Sl 68:20
Deut. 32:39Nu 12:13; 2Mb 21:18
Deut. 32:39Yer 17:14; Ho 6:1
Deut. 32:39Yes 43:13
Deut. 32:40Eks 6:8; Yes 45:23; Ahe 6:13
Deut. 32:40Sl 90:2; 1Ti 1:17; Chv 10:6
Deut. 32:41Sl 7:12; Eze 21:10
Deut. 32:41Yes 66:16; Nah 1:3
Deut. 32:41De 32:35; Yes 1:24; 59:18; 66:6; Nah 1:2
Deut. 32:41Eks 20:5
Deut. 32:42De 32:23
Deut. 32:42Yes 34:6; Eze 38:21
Deut. 32:42Yos 10:17, 26; 1Sa 15:33
Deut. 32:43Ge 12:3; 1Mf 8:43; Aro 3:29; 15:10
Deut. 32:432Mf 9:7; Chv 6:10
Deut. 32:43De 32:41; Mik 5:15; Lu 21:22
Deut. 32:44De 31:22; Chv 15:3
Deut. 32:44Nu 11:28; De 31:23
Deut. 32:46De 6:6; 11:18
Deut. 32:46De 6:7
Deut. 32:472Ti 3:16; Ahe 4:12
Deut. 32:47Le 18:5; De 30:19; Aro 10:5
Deut. 32:47Miy 3:2
Deut. 32:49Nu 27:12
Deut. 32:49De 34:1
Deut. 32:49Ge 10:19; 15:18; Yos 1:3
Deut. 32:50De 34:5
Deut. 32:50Nu 20:28; 33:38
Deut. 32:51Nu 20:12; 27:14
Deut. 32:51Nu 20:13
Deut. 32:51Le 10:3; 22:32; Yes 8:13; Mt 6:9
Deut. 32:52Nu 27:13; De 3:27; 34:4
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
  • 30
  • 31
  • 32
  • 33
  • 34
  • 35
  • 36
  • 37
  • 38
  • 39
  • 40
  • 41
  • 42
  • 43
  • 44
  • 45
  • 46
  • 47
  • 48
  • 49
  • 50
  • 51
  • 52
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 32:1-52

Deuteronomo

32 “Tamverani kumwamba inu, ndiloleni ndilankhule.

Ndipo dziko lapansi limve mawu a pakamwa panga.+

 2 Malangizo anga adzagwa ngati mvula,+

Mawu anga adzatsika ngati mame,+

Ngati mvula yowaza pa udzu,+

Ngatinso mvula yamphamvu pazomera.+

 3 Pakuti ndidzalengeza dzina la Yehova.+

Vomerezani ukulu wa Mulungu wathu!+

 4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+

Njira zake zonse ndi zolungama.+

Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita chosalungama.+

Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+

 5 Iwo achita okha zinthu zowawonongetsa,+

Si ana ake, chilemacho n’chawo.+

Iwo ndiwo m’badwo wopotoka maganizo ndi wokhotakhota!+

 6 Kodi mukupitiriza kuchitira Yehova mwa njira imeneyi,+

Anthu opusa ndi opanda nzeru inu?+

Kodi iye si Atate wanu amene anakulengani,+

Amene anakupangani ndi kukuchititsani kukhazikika?+

 7 Kumbukirani masiku akale,+

Ganizirani zaka za mibadwomibadwo ya m’mbuyomu.

Funsa bambo ako ndipo akuuza,+

Amuna achikulire pakati panu, ndipo akufotokozera.+

 8 Pamene Wam’mwambamwamba anapereka cholowa kwa mitundu,+

Pamene analekanitsa ana a Adamu,+

Anaika malire a anthu+

Poganizira chiwerengero cha ana a Isiraeli.+

 9 Pakuti gawo la Yehova ndilo anthu ake.+

Yakobo ndiye gawo la cholowa chake.+

10 Anam’peza m’dziko lachipululu,+

M’chipululu chopanda kanthu, molira zilombo zakutchire.+

Pamenepo anayamba kum’zungulira,+ kum’samalira,+

Kum’teteza monga mwana wa diso lake.+

11 Monga mmene chiwombankhanga chimagwedezera mwamphamvu chisa chake,

Mmene chimaulukira pamwamba pa ana ake,+

Mmene chimatambasulira mapiko ake, ndi kutenga anawo,

N’kuwanyamula pamapiko ake,+

12 Yehova yekha anapitiriza kumutsogolera,+

Ndipo panalibe mulungu wachilendo kuwonjezera pa iye.+

13 Anapitiriza kumuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+

Moti anadya zokolola za m’minda.+

Anapitirizanso kumudyetsa uchi wochokera m’thanthwe,+

Ndi mafuta ochokera m’mwala wa nsangalabwi.+

14 Anamudyetsanso mafuta a mkaka wa ng’ombe ndi mkaka wa nkhosa,+

Pamodzi ndi mafuta a nkhosa.

Anamudyetsa nkhosa zamphongo za ku Basana, mbuzi zamphongo,+

Pamodzi ndi tirigu wabwino koposa ngati mafuta okuta impso.+

Ndipo anali kumwa magazi a mphesa monga vinyo.+

15 Yesuruni*+ atayamba kunenepa, anayamba kupanduka.+

Iwe wanenepa, wakulupala, wakhuta mopitirira muyezo.+

Pamenepo iye anasiya Mulungu amene anam’panga,+

Ndi kunyoza Thanthwe+ la chipulumutso chake.

16 Anayamba kuputa nsanje+ yake ndi milungu yachilendo.+

Anapitiriza kumukhumudwitsa ndi zinthu zonyansa.+

17 Iwo anali kupereka nsembe kwa ziwanda, osati kwa Mulungu.+

Anapereka nsembe kwa milungu imene sanaidziwe,+

Milungu yatsopano yongobwera kumene,+

Imene makolo anu akale sanaidziwe.

18 Munaiwala Thanthwe limene linakuberekani,+

Ndipo munayamba kuiwala Mulungu amene anachititsa kuti mukhalepo kudzera mwa zowawa za pobereka.+

19 Yehova ataona zimenezi anayamba kuwanyoza,+

Chifukwa chakuti ana ake aamuna ndi aakaziwo anam’sautsa.

20 Choncho iye anati, ‘Ndiwabisire nkhope yanga,+

Ndione kuti ziwathera bwanji.

Pakuti iwo ndi m’badwo wokonda zoipa,+

Ana osakhulupirika.+

21 Iwo andichititsa nsanje ndi milungu yachabe.+

Andisautsa ndi mafano awo opanda pake.+

Ndipo ine ndidzawachititsa nsanje ndi anthu achabe,+

Ndidzawakhumudwitsa ndi mtundu wopusa.+

22 Pakuti pa kukwiya kwanga moto wayaka,+

Ndipo udzayaka mpaka kukafika ku Manda,* malo a pansi penipeni.+

Udzanyeketsa dziko lapansi ndi zipatso zake,+

Ndi kuyatsa maziko a mapiri.+

23 Ndidzawonjezera masoka awo,+

Mivi yanga ndidzaithera pa iwo.+

24 Adzalefuka ndi njala+ ndi kuwonongeka ndi matenda otentha thupi koopsa,+

Ndi chiwonongeko chowawa.+

Ndidzawatumizira zilombo za mano ataliatali,+

Pamodzi ndi njoka zapoizoni za m’fumbi.+

25 Kunja lupanga lidzawasandutsa anamfedwa,+

Ndipo mkati mwa nyumba, mantha adzawasandutsa anamfedwa.+

Zimenezi zidzawaphera anyamata ndi anamwali,+

Mwana woyamwa pamodzi ndi munthu wa imvi.+

26 Ndikananena kuti: “Ndidzawabalalitsa,+

Ndidzachititsa anthu kuti asatchule n’komwe za iwo,”+

27 Ngati ndikanati sindikuopa kusautsidwa ndi mdani,+

Kuti adani awo angamve molakwa,+

Kutinso anganene kuti: “Dzanja lathu lapambana,+

Ndipo si Yehova amene wachita zonsezi.”+

28 Pakuti iwo ndi mtundu wopanda nzeru,+

Ndipo ndi osazindikira.+

29 Akanakhala anzeru,+ akanaganizira mozama zimenezi.+

Akanalingalira kuti ziwathera bwanji.+

30 Kodi munthu mmodzi angathamangitse bwanji anthu 1,000,

Kapena anthu awiri angapitikitse bwanji anthu 10,000?+

N’zosatheka, pokhapokha Thanthwe lawo litawagulitsa,+

Komanso ngati Yehova atawapereka.

31 Pakuti thanthwe lawo silofanana ndi Thanthwe lathu,+

Ndipo adani athu angavomereze zimenezi.+

32 Mtengo wawo wa mpesa ndi wochokera ku mtengo wa mpesa wa ku Sodomu,

Ndi kuminda ya m’mapiri a ku Gomora.+

Zipatso zawo za mphesa ndi zakupha,

Ndipo ndi zowawa.+

33 Vinyo wawo ndi poizoni wa njoka zikuluzikulu,

Ndiponso ndi poizoni wakupha wa mamba.+

34 Kodi sindinasunge zimenezi,

Ndi kuziikira chidindo m’nkhokwe yanga?+

35 Kubwezera ndi kwanga, chilangonso ndi changa.+

Pa nthawi yoikidwiratu phazi lawo lidzaterereka poyenda,+

Pakuti tsiku la tsoka lawo layandikira,+

Ndipo zowagwera zikufika mofulumira.’+

36 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ake,+

Ndipo adzamva chisoni chifukwa cha atumiki ake,+

Chifukwa adzaona kuti thandizo lawachokera.

Adzaona kuti pangokhala munthu wonyozeka ndi wopanda pake.

37 Pamenepo iye adzati, ‘Ili kuti milungu yawo,+

Thanthwe limene anathawirako,+

38 Milungu imene inali kudya mafuta a nsembe zawo,+

Ndi kumwa vinyo wa nsembe zawo zachakumwa?+

Ibwere kudzakuthandizani.+

Ikhaletu malo anu obisalamo.+

39 Onani tsopano kuti ndine Mulungu,+

Ndipo palibe milungu ina pamodzi ndi ine.+

Ndimapha ndiponso ndimapereka moyo.+

Ndavulaza koopsa,+ ndipo ine ndidzachiritsa,+

Palibe aliyense wonditsomphola m’dzanja langa.+

40 Ndikukweza dzanja langa kumwamba polumbira,+

Ndipo ndikunena kuti: “Pali ine, Mulungu wamoyo wosatha,”+

41 Ndikanoladi lupanga langa lonyezimira,+

Dzanja langa likagwira chiweruzo,+

Ndidzalipsira adani anga,+

Ndipo ndidzabwezera chilango kwa odana nane kwambiri.+

42 Ndidzaledzeretsa mivi yanga ndi magazi,+

Magazi a anthu ophedwa ndi ogwidwa.

Ndipo lupanga langa lidzadya nyama,+

Pamodzi ndi mitu ya atsogoleri a adani.’+

43 Kondwerani, mitundu inu, pamodzi ndi anthu ake,+

Pakuti adzabwezera magazi a atumiki ake,+

Ndipo adzabwezera chilango kwa adani ake,+

Nadzaphimba machimo a dziko la anthu ake.”

44 Pamenepo Mose anabwera ndi kulankhula mawu onse a nyimbo iyi m’makutu mwa anthu onse,+ iye pamodzi ndi Hoseya* mwana wa Nuni.+ 45 Mose atamaliza kulankhula mawu onsewa kwa Aisiraeli onse, 46 anapitiriza kuwauza kuti: “Ganizirani mofatsa mawu onse amene ndikulankhula mokuchenjezani lero,+ ndipo muuze ana anu kuti aonetsetse kuti akuchita zimene mawu onse a chilamulo ichi akunena.+ 47 Pakuti amenewa si mawu opanda pake kwa inu,+ chifukwa mawu amenewa ndiwo moyo wanu.+ Mwa kutsatira mawu amenewa mudzatalikitsa masiku anu panthaka imene mukupita kukaitenga kukhala yanu, mutawoloka Yorodano.”+

48 Yehova anapitiriza kulankhula ndi Mose pa tsiku lomweli kuti: 49 “Kwera m’phiri ili la Abarimu,+ phiri la Nebo,+ limene lili m’dziko la Mowabu, moyang’anana ndi Yeriko, ndipo uone dziko la Kanani limene ndikupereka kwa ana a Isiraeli kuti likhale lawo.+ 50 Pamenepo ukafera m’phiri limene ukukwera ndi kugona ndi makolo ako,+ monga mmene Aroni m’bale wako anafera m’phiri la Hora+ ndi kugona ndi makolo ake. 51 Izi zili choncho chifukwa anthu inu munachita mosakhulupirika kwa ine+ pakati pa ana a Isiraeli, kumadzi a pa Meriba+ ku Kadesi, m’chipululu cha Zini. Ndiponso chifukwa chakuti anthu inu simunandilemekeze pakati pa ana a Isiraeli.+ 52 Pakuti udzaona dzikolo uli patali, koma sudzalowa m’dziko limene ndikupereka kwa ana a Isiraeli.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena