Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mwanayo atabadwa, Leya anati: “Mulungu wandipatsa mphoto chifukwa ndapereka kapolo wanga kwa mwamuna wanga.” Chotero Leya anatcha mwanayo dzina lakuti Isakara.*+

  • Genesis 46:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana a Isakara+ anali Tola,+ Puva,+ Yabi ndi Simironi.+

  • Numeri 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kumbali yake imodzi azimangako a fuko la Isakara.+ Mtsogoleri wa ana a Isakara ndi Netaneli,+ mwana wa Zuwara.

  • Numeri 26:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ana aamuna a Isakara+ ndi mabanja awo anali awa: Tola+ amene anali kholo la banja la Atola, Puva amene anali kholo la banja la Apuna,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena