Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Nkhosayo muisunge kufikira tsiku la 14 la mwezi uno.+ Kenako banja lililonse la Isiraeli lidzaphe nkhosa yawo madzulo kuli kachisisira.*+

  • Levitiko 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 M’mwezi woyamba,* pa tsiku la 14 m’mweziwo,+ madzulo kuli kachisisira,* lizikhala tsiku la pasika+ wa Yehova.

  • Numeri 28:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “‘M’mwezi woyamba, pa tsiku la 14, pazikhala pasika wa Yehova.+

  • Deuteronomo 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Muzisunga mwambo wa m’mwezi wa Abibu*+ pochita chikondwerero cha pasika kwa Yehova Mulungu wanu,+ chifukwa m’mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani mu Iguputo usiku.+

  • Yoswa 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ana a Isiraeliwo anakhalabe ku Giligala. Anachita pasika madzulo pa tsiku la 14 la mweziwo,+ ali m’chipululu cha Yeriko.

  • Maliko 14:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsopano pa tsiku loyamba la chikondwerero cha mikate yopanda chofufumitsa,+ pamene mwa mwambo anali kupereka nsembe nyama ya pasika, ophunzira ake+ anamufunsa kuti: “Kodi mukufuna tipite kuti kumene tikakukonzereni malo odyerako pasika?”+

  • 1 Akorinto 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chotsani chofufumitsa chakalecho, kuti mukhale mtanda watsopano,+ popeza ndinu opanda chofufumitsa. Pakuti Khristu+ waperekedwa+ monga nsembe yathu ya pasika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena