-
Salimo 78:42Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
42 Iwo sanakumbukire dzanja la Mulungu,+
Sanakumbukire tsiku limene anawawombola kwa mdani wawo,+
-
Yohane 12:37Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
37 Koma ngakhale kuti anachita zizindikiro zambiri pamaso pawo, iwo sanali kukhulupirira iye,
-
-
-