Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Uike Aroni ndi ana ake kukhala ansembe, kuti azigwira ntchito yaunsembe.+ Aliyense amene si Mlevi akayandikira malowo, aziphedwa.”+

  • Numeri 3:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Amene anali kumanga msasa wawo kum’mawa kwa chihema chopatulika, kumbali yotulukira dzuwa, anali Mose ndi Aroni, ndiponso ana a Aroni. Ntchito yawo inali kutumikira m’malo opatulika,+ kutumikira ana a Isiraeli. Aliyense amene si Mlevi akayandikira malowo, anayenera kuphedwa.+

  • Numeri 16:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 “Amuna inu, chokani pakati pa khamuli kuti ndilifafanize kamodzi n’kamodzi.”+ Atamva zimenezi, iwo anagwada n’kuwerama mpaka nkhope zawo pansi.+

  • Salimo 73:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Haa! M’kanthawi kochepa, iwo akhala chinthu chodabwitsa.+

      Afika pamapeto awo ndipo atha chifukwa cha masoka owagwera modzidzimutsa!

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena