Numeri 11:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Tsopano anthuwo anayamba kudandaula pamaso pa Yehova ngati kuti anali pamavuto.+ Yehova atamva kudandaulako anawapsera mtima, ndipo moto wa Yehova unawayakira n’kupsereza ena a iwo kumalire a msasa.+ Numeri 14:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 “Kodi khamu la anthu oipa amenewa lidandaula motsutsana nane kufikira liti?+ Ndamva kudandaula konseko kumene ana a Isiraeli akuchita motsutsana nane.+ Numeri 16:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Zimene mukuchitazi, iweyo limodzi ndi khamu lako lonseli, mukuukira Yehova.+ Kunena za Aroni, kodi iye ndani kuti amuna inu mum’dandaule?”+ Numeri 16:41 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 41 Koma tsiku lotsatira, khamu lonse la ana a Isiraeli linayamba kung’ung’udza motsutsana ndi Mose ndi Aroni,+ kuti: “Mwapha anthu a Yehova inu.” 1 Akorinto 10:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Tisakhalenso ong’ung’udza, mmene ena mwa iwo anang’ung’udzira,+ wowonongayo+ n’kuwawononga onsewo.
11 Tsopano anthuwo anayamba kudandaula pamaso pa Yehova ngati kuti anali pamavuto.+ Yehova atamva kudandaulako anawapsera mtima, ndipo moto wa Yehova unawayakira n’kupsereza ena a iwo kumalire a msasa.+
27 “Kodi khamu la anthu oipa amenewa lidandaula motsutsana nane kufikira liti?+ Ndamva kudandaula konseko kumene ana a Isiraeli akuchita motsutsana nane.+
11 Zimene mukuchitazi, iweyo limodzi ndi khamu lako lonseli, mukuukira Yehova.+ Kunena za Aroni, kodi iye ndani kuti amuna inu mum’dandaule?”+
41 Koma tsiku lotsatira, khamu lonse la ana a Isiraeli linayamba kung’ung’udza motsutsana ndi Mose ndi Aroni,+ kuti: “Mwapha anthu a Yehova inu.”
10 Tisakhalenso ong’ung’udza, mmene ena mwa iwo anang’ung’udzira,+ wowonongayo+ n’kuwawononga onsewo.