Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndipo mawu awa amene ndikukulamula lero azikhala pamtima pako,+

  • Salimo 78:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Kuti anawo azidzadalira Mulungu,+

      Ndi kuti asadzaiwale zochita za Mulungu+ koma kuti azidzasunga malamulo ake.+

  • Salimo 119:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  34 Ndithandizeni kukhala wozindikira kuti nditsatire chilamulo chanu,+

      Ndiponso kuti ndichisunge ndi mtima wonse.+

  • 1 Yohane 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chifukwa kukonda+ Mulungu kumatanthauza kusunga malamulo ake, ndipo malamulo akewo+ ndi osalemetsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena