Deuteronomo 12:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Samalani kuti musadzapereke nsembe zanu zopsereza pamalo ena alionse amene mungaone.+ Deuteronomo 12:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Ukatero uzipereka nsembe zako zopsereza,+ nyama ndi magazi,+ paguwa lansembe la Yehova Mulungu wako. Magazi a nsembe zako uziwathira pansi pafupi ndi guwa lansembe la Yehova+ Mulungu wako, koma nyamayo utha kuidya. Yoswa 22:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Kenako ana ena a Isiraeli anauzidwa+ kuti: “Tamverani! Ana a Rubeni, ana a Gadi, ndi hafu ya fuko la Manase amanga guwa lansembe m’malire a dziko la Kanani, m’chigawo cha Yorodano kumbali ya ana a Isiraeli.” 1 Mafumu 12:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Choncho mfumuyo inakambirana ndi anthu ena+ n’kupanga ana awiri a ng’ombe agolide.+ Itatero inauza anthuwo kuti: “N’zovuta kwambiri kwa inu kuti muzipita ku Yerusalemu. Nayu Mulungu wanu+ Aisiraeli inu, amene anakutulutsani m’dziko la Iguputo.”+
27 Ukatero uzipereka nsembe zako zopsereza,+ nyama ndi magazi,+ paguwa lansembe la Yehova Mulungu wako. Magazi a nsembe zako uziwathira pansi pafupi ndi guwa lansembe la Yehova+ Mulungu wako, koma nyamayo utha kuidya.
11 Kenako ana ena a Isiraeli anauzidwa+ kuti: “Tamverani! Ana a Rubeni, ana a Gadi, ndi hafu ya fuko la Manase amanga guwa lansembe m’malire a dziko la Kanani, m’chigawo cha Yorodano kumbali ya ana a Isiraeli.”
28 Choncho mfumuyo inakambirana ndi anthu ena+ n’kupanga ana awiri a ng’ombe agolide.+ Itatero inauza anthuwo kuti: “N’zovuta kwambiri kwa inu kuti muzipita ku Yerusalemu. Nayu Mulungu wanu+ Aisiraeli inu, amene anakutulutsani m’dziko la Iguputo.”+