-
Salimo 105:44Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
44 Pang’onopang’ono anawapatsa mayiko a anthu a mitundu ina,+
Ndipo zipatso za ntchito imene mitundu ya anthu inagwira mwakhama, anazitenga kukhala zawo,+
-