Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Muzichita mdulidwe kuti ukhale chizindikiro cha pangano la pakati pa ine ndi inu.+

  • Ekisodo 4:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Zitatero, Zipora+ anatenga mwala wakuthwa n’kudula khungu+ la mwana wakeyo. Ndipo khungu analidulalo analiponya pamapazi ake n’kunena kuti: “Popeza ndinu mkwati wa magazi kwa ine.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena