Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno zimene zinali kuchitika n’zakuti, Mose akangokweza dzanja lake m’mwamba, Aisiraeli anali kupambana pankhondoyo,+ koma akangotsitsa dzanja lake, Aamaleki anali kupambana.

  • Yoswa 8:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zikakatero, inu mukavumbuluke ndi kukalanda mzindawo, pakuti Yehova Mulungu wanu adzaupereka ndithu m’manja mwanu.+

  • Yoswa 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndipo Yoswa sanatsitse mkono wake umene anautambasula polozetsa nthungo+ kumzindawo, mpaka anthu onse a ku Ai ataphedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena