Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno zimene zinali kuchitika n’zakuti, Mose akangokweza dzanja lake m’mwamba, Aisiraeli anali kupambana pankhondoyo,+ koma akangotsitsa dzanja lake, Aamaleki anali kupambana.

  • Yoswa 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Tsopano Yehova anauza Yoswa kuti: “Lozetsa nthungo* imene ili m’dzanja lako ku Ai,+ pakuti mzindawo ndaupereka m’manja mwako.”+ Chotero Yoswa analozetsa kumzindawo nthungo imene inali m’dzanja lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena